CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Zimene Yobu Anachita Kuti Akhalebe Woyera
Yobu anachita pangano ndi maso ake (Yob 31:1; w10 4/15 21 ¶8)
Yobu ankadziwa bwino mavuto amene angakhalepo chifukwa chochita zoipa (Yob 31:2, 3; w08 9/1 11 ¶4)
Yobu ankakumbukira kuti Mulungu amaona zimene iye amachita (Yob 31:4; w10 11/15 5-6 ¶15-16)
Kukhala woyera kumatanthauza kulankhula komanso kuchita zinthu zoyenera. Koma si zokhazi, timafunikanso kukhala oyera mumtima.—Mt 5:28.