Onani zimene zilipo

Zida zophunzilila Baibo

Laibulale yathu ya Zida zophunzilila Baibo kwaulele komanso zofalitsa zina, ingakuthandizeni kukulitsa cidwi canu cocita phunzilo la munthu mwini, komanso kuonjezela cidziwitso canu pa Mawu a Mulungu. Seŵenzetsani Baibo ya pa intaneti imene ili na zida zambili monga mavidiyo, mapu, kalozela wa mawu a m’Baibo, na zida zina.

Ŵelengani Baibo pa Intaneti

Onani mbali zosiyanasiyana za Baibo ya Cimasulilo ca Dziko Latsopano, Baibo imene ni yolondola komanso yosavuta kuŵelenga.

Mavidiyo Othandiza Kuphunzila Baibo

Mfundo Zothandiza Kumvetsa Mabuku a m’Baibo

Nkhani za m’mabuku a m’Baibo komanso mmene zinthu zinalili pamene bukulo linali kulembedwa

Zimene Baibo Imaphunzitsa

Mavidiyo amenewa ali na mayankho a mafunso ofunika kwambili a m’Baibo monga akuti: N’cifukwa ciyani Mulungu analenga dziko lapansi? Kodi akufa ali mu mkhalidwe wabwanji? N’cifukwa ciyani Mulungu amalola kuti anthu azivutika?

Mabuku Ophunzilila Baibo na Malifalensi

Kuyankha Mafunso a m’Baibo

Pezani mayankho ocokela m’Baibo okhudza Mulungu, Yesu, banja, mavuto komanso ena ambili.

Laibulali ya pa Intaneti (opens new window)

Pezani nkhani za m’Baibo pa Intaneti m’mabuku a Mboni za Yehova.

Pezani Wokuphunzitsani Baibo

Kodi Phunzilo la Baibulo N’ciani?

Pezani mayankho a mafunso okhudza mmene timacitila phunzilo la Baibulo laulele.

Pemphani kuti wa Mboni adzakucezeleni

Kambilanani nkhani ya m’Baibo na Mboni za Yehova, kapena laŵani maphunzilo a Baibo amene timapeleka.